Thandizo

Apr 13, 2023
25 mins

Episode Description

Koma pamene wafika Nkhoswe, amene Ine ndidzamtuma kwa inu kuchokera kwa Atate, ndiye Mzimu wa chowonadi amene atuluka kwa Atate, Iyeyu adzandichitira Ine umboni. Ndipo inunso mudzachitira umboni, chifukwa mudali ndi Ine kuyambira pachiyambi.

(Joh 15:26-27)

See all episodes

Never lose your place, on any device

Create a free account to sync, back up, and get personal recommendations.